Masalimo 112:3 - Buku Lopatulika3 M'nyumba mwake mudzakhala akatundu ndi chuma: Ndi chilungamo chake chikhala chikhalire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 M'nyumba mwake mudzakhala akatundu ndi chuma: Ndi chilungamo chake chikhala chikhalire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Banja lake lidzakhala lachuma ndi lolemera, ndipo kulungama kwake kudzakhala kwamuyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kulemera ndi chuma zili mʼnyumba yake, ndipo chilungamo chake ndi chosatha. Onani mutuwo |