Masalimo 112:2 - Buku Lopatulika2 Mbeu yake idzakhala yamphamvu padziko lapansi; mbadwo wa oongoka mtima udzadalitsidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mbeu yake idzakhala yamphamvu pa dziko lapansi; mbadwo wa oongoka mtima udzadalitsidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Zidzukulu zake zidzakhala zamphamvu pa dziko lapansi. Ana a munthuyo adzakhala odala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ana ake adzakhala amphamvu mʼdziko; mʼbado wa olungama mtima udzadalitsidwa. Onani mutuwo |