Genesis 26:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Isaki anabzala m'dzikomo, nalandira za makumi khumi chaka chimenecho; ndipo Yehova anamdalitsa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Isaki anabzala m'dzikomo, nalandira za makumi khumi chaka chimenecho; ndipo Yehova anamdalitsa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Isaki adabzala mbeu m'dzikomo, ndipo chaka chimenecho adakolola dzinthu dzochuluka koposa, chifukwa Chauta adaamudalitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Isake anadzala mbewu mʼmunda, ndipo chaka chomwecho anakolola zinthu zambiri chifukwa Yehova anamudalitsa. Onani mutuwo |