Genesis 26:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Abimeleki anauza anthu ake, nati, Aliyense amene akhudza mwamuna uyo kapena mkazi wake, zoonatu adzaphedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Abimeleki anauza anthu ake, nati, Aliyense amene akhudza mwamuna uyo kapena mkazi wake, zoonatu adzaphedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono Abimeleki adalamula anthu ake onse kuti, “Musamuchite kanthu munthuyu pamodzi ndi mkazi wake yemwe. Wina aliyense akangotero, aphedwa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Choncho Abimeleki analamula anthu ake onse nati, “Aliyense amene avutitse munthu uyu pamodzi ndi mkazi wake adzaphedwa ndithu.” Onani mutuwo |