Genesis 26:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo analemera munthuyo, nalemera ndithu kufikira kuti anakhala wolemera kwambiri: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo analemera munthuyo, nalemera ndithu kufikira kuti anakhala wolemera kwambiri: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Chuma chake chidanka chichulukirachulukira, ndipo adasanduka munthu wolemera kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Isake analemera. Chuma chake chinkachulukirachulukira mpaka anasanduka munthu wolemera kwambiri. Onani mutuwo |