Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 2:12 - Buku Lopatulika

golide wa dziko ali wabwino; ndimonso muli bedola ndi mwala wasohamu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

golide wa dziko ali wabwino; ndimonso muli bedola ndi mwala wasohamu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

(Golide wakumeneko ndi wabwino. Kumapezekanso bedeliyo ndi miyala ya mtengowapatali yotchedwa onikisi.)

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

(Golide wa ku dziko ili ndi wabwino. Kulinso miyala yokongola ya bedola ndi onikisi).

Onani mutuwo



Genesis 2:12
8 Mawu Ofanana  

Dzina la woyamba ndi Pisoni: umenewo ndiwo wozungulira dziko lonse la Havila, m'mene muli golide;


Dzina la mtsinje wachiwiri ndi Gihoni: umenewo ndiwo wozungulira dziko lonse la Kusi.


Sailinganiza ndi golide wa Ofiri, ndi sohamu wa mtengo wake wapatali kapena safiro.


miyala yaberulo, ndi miyala yoika paefodi, ndi pachapachifuwa.


ndi mzere wachinai wa tarisisi, sohamu, ndi yasefe; zikhale zogwirika ndi golide m'zoikamo zao.


Ndi mzere wachinai wa tarisisi, sohamu, ndi yasefe; inakhala yogwirika ndi golide maikidwe ake.


Unali mu Edeni, munda wa Mulungu, mwala uliwonse wa mtengo wake unali chofunda chako, sardiyo, topazi, diamondi, berulo, sohamu, ndi yaspi, safiro, nofeki, bareketi, ndi golide; malingaka ako ndi akazi ako anakutumikira tsiku lolengedwa iwe zinakonzekeratu.


Ndipo mana ananga zipatso zampasa, ndi maonekedwe ake ngati maonekedwe a bedola.