Eksodo 25:7 - Buku Lopatulika7 miyala yaberulo, ndi miyala yoika paefodi, ndi pachapachifuwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 miyala yaberulo, ndi miyala yoika paefodi, ndi pachapachifuwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ulandirenso miyala yokoma ya onikisi, ndiponso miyala ina yoti uike pa chovala chaunsembe cha efodi, ndi pa chovala chapachifuwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 miyala yokongola ya mtundu wa onikisi ndi ina yabwino yoyika pa efodi ndi pa chovala cha pachifuwa. Onani mutuwo |