Eksodo 25:6 - Buku Lopatulika6 mafuta akuunikira, zonunkhira za mafuta odzoza, ndi za chofukiza cha fungo lokoma; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 mafuta akuunikira, zonunkhira za mafuta odzoza, ndi za chofukiza cha fungo lokoma; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 mafuta a nyale, zonunkhira za mafuta odzozera, ndiponso lubani wa fungo lokoma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 mafuta anyale a olivi, zonunkhiritsa mafuta odzozera ndi zopangira lubani wonunkhira; Onani mutuwo |