Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 25:6 - Buku Lopatulika

6 mafuta akuunikira, zonunkhira za mafuta odzoza, ndi za chofukiza cha fungo lokoma;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 mafuta akuunikira, zonunkhira za mafuta odzoza, ndi za chofukiza cha fungo lokoma;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 mafuta a nyale, zonunkhira za mafuta odzozera, ndiponso lubani wa fungo lokoma.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 mafuta anyale a olivi, zonunkhiritsa mafuta odzozera ndi zopangira lubani wonunkhira;

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 25:6
7 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipanga nyali zake, zisanu ndi ziwiri; ndipo ayatse nyali zake, ziwale pandunji pake.


ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Ndipo uuze ana a Israele akutengere mafuta a azitona oyera opera akuunikira, kuti awalitse nyali kosalekeza.


Napanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi mkuwa.


Ndipo zoyang'anira Eleazara, mwana wa Aroni wansembe, ndizo mafuta a nyaliyo, ndi chofukiza cha fungo lokoma, ndi nsembe yaufa kosalekeza, ndi mafuta odzoza, udikiro wa chihema chonse, ndi zonse zili m'mwemo, malo opatulika, ndi zipangizo zake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa