Eksodo 25:5 - Buku Lopatulika5 ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 zikopa zankhosa zonyika mu utoto wofiira, zikopa zofeŵa, matabwa a mtengo wa kasiya, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 zikopa za nkhosa zazimuna za utoto wofiira ndi zikopa za akatumbu; matabwa amtengo wa mkesha; Onani mutuwo |