Eksodo 25:4 - Buku Lopatulika4 ndi lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ndi ubweya wa mbuzi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 ndi lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ndi ubweya wa mbuzi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 nsalu zobiriŵira, zofiirira ndi zofiira, nsalu zokoma zathonje, nsalu zopangidwa ndi ubweya wambuzi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Nsalu zobiriwira, zapepo, zofiira, nsalu zofewa, ubweya wambuzi; Onani mutuwo |