Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 25:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo choperekacho uchilandire kwa iwo ndi ichi: golide, ndi siliva, ndi mkuwa,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo choperekacho uchilandire kwa iwo ndi ichi: golide, ndi siliva, ndi mkuwa,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Zopereka zimene ulandirezo ndi izi: golide, siliva, mkuŵa,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Zopereka zimene ulandire kwa anthuwo ndi izi: Golide, siliva ndi mkuwa.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 25:3
5 Mawu Ofanana  

Chitsulo achitenga m'nthaka, ndi mkuwa ausungunula kumwala.


Lankhula ndi ana a Israele, kuti anditengere chopereka; ulandire chopereka changa kwa munthu aliyense mtima wake umfunitsa mwini.


ndi lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ndi ubweya wa mbuzi;


Ndipo atenge golide, ndi lamadzi ndi lofiirira ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa.


dziko loti mudzadyamo mkate wosapereweza; simudzasowamo kanthu; dziko loti miyala yake nja chitsulo, ndi m'mapiri ake mukumbe mkuwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa