Eksodo 36:1 - Buku Lopatulika
Pamenepo anachita Bezalele ndi Oholiyabu, ndi anthu aluso, amene Yehova adaika luso ndi nzeru m'mtima mwao adziwe machitidwe ake a ntchito yonse ya utumiki wake wa malo opatulika, monga mwa zonse adauza Yehova.
Onani mutuwo
Pamenepo anachita Bezalele ndi Oholiyabu, ndi anthu aluso, amene Yehova adaika luso ndi nzeru m'mtima mwao adziwe machitidwe ake a ntchito yonse ya utumiki wake wa malo opatulika, monga mwa zonse adauza Yehova.
Onani mutuwo
“Ndipo Bezalele, Oholiyabu, pamodzi ndi aluso onse amene Chauta adaŵapatsa luso ndi nzeru zodziŵira kupanga zofunika zonse zomangira malo opatulika, adzapanga zonse iwowo, monga momwe Chauta adalamulira.”
Onani mutuwo
Choncho Bezaleli, Oholiabu pamodzi ndi anthu aluso onse amene Yehova anawapatsa luso ndi nzeru zodziwira kupanga zofunika zonse zomangira malo opatulika, adzapanga zonse iwowo, monga momwe Yehova analamulira.”
Onani mutuwo