Eksodo 12:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo anthu anawerama, nalambira. Ndipo ana a Israele anamuka nachita monga Yehova adalamulira Mose ndi Aroni; anachita momwemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo anthu anawerama, nalambira. Ndipo ana a Israele anamuka nachita monga Yehova adalamulira Mose ndi Aroni; anachita momwemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Aisraele adapita, ndipo adamvera zimenezo. Adachitadi zonse zimene Chauta adalamula Mose ndi Aroni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Aisraeli anachita monga momwe Yehova analamulira Mose ndi Aaroni. Onani mutuwo |