Eksodo 31:11 - Buku Lopatulika11 ndi mafuta odzoza, ndi chofukiza cha zonunkhira zokoma za malo opatulika; azichita monga mwa zonse ndakuuza iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 ndi mafuta odzoza, ndi chofukiza cha zonunkhira zokoma za malo opatulika; azichita monga mwa zonse ndakuuza iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 mafuta odzozera ndiponso lubani wa fungo lokoma, zonsezo zokhalira malo oyera. Adzapange zinthu zonsezi monga ndakulamulira iwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 ndiponso mafuta odzozera ndi lubani wonunkhira wa ku malo opatulika. Iwo azipanga monga momwe Ine ndinakulamulira.” Onani mutuwo |