Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 13:4 - Buku Lopatulika

Mutuluka lero lino mwezi wa Abibu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mutuluka lero lino mwezi wa Abibu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mukuchoka ku Ejipito pa tsiku lalero, mwezi uno wa Abibu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa tsiku la lero mwezi uno wa Abibu, mukutuluka mʼdziko la Igupto.

Onani mutuwo



Eksodo 13:4
6 Mawu Ofanana  

Koma iwo adzabweranso kuno mbadwo wachinai: pakuti mphulupulu za Aamori sizinakwaniridwe.


Mwezi uno uzikhala kwa inu woyamba wa miyezi; muziuyesa mwezi woyamba wa chaka.


Uzisunga chikondwerero cha Mkate wopanda chotupitsa; masiku asanu ndi awiri uzidya mkate wopanda chotupitsa, monga ndinakuuza, nyengo yoikika, mwezi wa Abibu, pakuti m'menemo unatuluka mu Ejipito; koma asaoneke munthu pamaso panga opanda kanthu;


Uzisunga chikondwerero cha Mkate wopanda chotupitsa. Uzidya mkate wopanda chotupitsa masiku asanu ndi awiri, monga ndakuuza pa nthawi yonenedwa, m'mwezi wa Abibu; pakuti mwezi wa Abibu unatuluka mu Ejipito.


Ndipo ndinakhazikitsanso nao chipangano changa, kuwapatsa dziko la Kanani, dziko la maulendo ao, anali alendo m'mwemo.