Genesis 15:16 - Buku Lopatulika16 Koma iwo adzabweranso kuno mbadwo wachinai: pakuti mphulupulu za Aamori sizinakwaniridwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma iwo adzabweranso kuno mbadwo wachinai: pakuti mphulupulu za Aamori sizinakwaniridwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Patapita mibadwo inai, zidzukulu zakozo zidzabwereranso, chifukwa sindidzaŵathamangitsa Aamori mpaka kuipa kwao kutafika pachimake penipeni kuti adzalangidwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Patapita mibado inayi, adzukulu ako adzabwereranso kuno popeza tchimo la Aamori silinafike pachimake kuti alangidwe.” Onani mutuwo |