Genesis 15:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo iwe udzanka kwa makolo ako m'mtendere; nudzaikidwa ndi ukalamba wabwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo iwe udzanka kwa makolo ako m'mtendere; nudzaikidwa ndi ukalamba wabwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsono iwe udzakhala ndi moyo nthaŵi yaitali ndipo udzafa mwamtendere. Udzaikidwa m'manda utakalamba kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Komabe iweyo udzamwalira mu mtendere ndi kuyikidwa mʼmanda utakalamba bwino. Onani mutuwo |