Genesis 15:14 - Buku Lopatulika14 ndiponso mtunduwo adzautumikira, Ine ndidzauweruza: ndiponso pambuyo pake adzatuluka ndi chuma chambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 ndiponso mtunduwo adzautumikira, Ine ndidzauweruza: ndiponso pambuyo pake adzatuluka ndi chuma chambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma mtundu umene udzachite zimenezi, ndidzaulanga, ndipo zidzukulu zakozo potuluka m'dzikomo, zidzatenga chuma chambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma ndidzalanga dziko limene zidzukulu zako zidzagwireko ukapolo ndipo pambuyo pake iwo adzatulukamo ndi chuma chambiri. Onani mutuwo |