Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 13:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Pa tsiku la lero mwezi uno wa Abibu, mukutuluka mʼdziko la Igupto.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

4 Mutuluka lero lino mwezi wa Abibu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Mutuluka lero lino mwezi wa Abibu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Mukuchoka ku Ejipito pa tsiku lalero, mwezi uno wa Abibu.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 13:4
6 Mawu Ofanana  

Patapita mibado inayi, adzukulu ako adzabwereranso kuno popeza tchimo la Aamori silinafike pachimake kuti alangidwe.”


“Mwezi uno uzikhala mwezi wanu woyamba wa chaka.


“Muzichita Chikondwerero cha Buledi wopanda Yisiti. Kwa masiku asanu ndi awiri muzidya buledi wopanda yisiti monga ndinakulamulirani. Muzichita zimenezi mwezi wa Abibu pa nthawi yomwe ndayika, pakuti mʼmwezi umenewu munatuluka mʼdziko la Igupto. “Pasapezeke munthu wobwera pamaso panga wopanda kanthu mʼmanja.


“Muzichita chikondwerero cha buledi wopanda yisiti. Kwa masiku asanu ndi awiri muzidya buledi wopanda yisiti monga momwe ndinakulamulirani. Muzichita zimenezi pa nthawi yoyikika mwezi wa Abibu, pakuti mwezi umenewu inu munatuluka mʼdziko la Igupto.


Ndinakhazikitsa pangano langa ndi iwo kuwalonjeza kuti ndidzawapatsa dziko la Kanaani kumene anakhalako kale ngati alendo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa