Eksodo 6:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo ndinakhazikitsanso nao chipangano changa, kuwapatsa dziko la Kanani, dziko la maulendo ao, anali alendo m'mwemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo ndinakhazikitsanso nao chipangano changa, kuwapatsa dziko la Kanani, dziko la maulendo ao, anali alendo m'mwemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndidachita nawo chipangano ndi kuŵalonjeza kuti ndidzaŵapatsa dziko la Kanani, momwe adakhalamo kale ngati alendo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndinakhazikitsa pangano langa ndi iwo kuwalonjeza kuti ndidzawapatsa dziko la Kanaani kumene anakhalako kale ngati alendo. Onani mutuwo |