Eksodo 6:5 - Buku Lopatulika5 Ndamvanso kubuula kwa ana a Israele, amene Aejipito awayesa akapolo; ndipo ndakumbukira chipangano changa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndamvanso kubuula kwa ana a Israele, amene Aejipito awayesa akapolo; ndipo ndakumbukira chipangano changa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsopano ndamva kudandaula kwa Aisraele, amene ali mu ukapolo wa Aejipito, ndipo ndakumbukira chipangano changa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndamvanso kubuwula kwa Aisraeli, amene Aigupto awayesa akapolo ndipo ndakumbukira pangano langa.” Onani mutuwo |