Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 6:9 - Buku Lopatulika

Momwemo mfumu Dariusi anatsimikiza cholembedwa ndi choletsacho.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Momwemo mfumu Dariusi anatsimikiza cholembedwa ndi choletsacho.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho mfumu Dariyo anasindikizapo dzina lake pa lamuloli.

Onani mutuwo



Danieli 6:9
6 Mawu Ofanana  

Chikakomera mfumu, atuluke mau achifumu pakamwa pake, nalembedwe m'malamulo a Apersiya ndi Amediya, angasinthike, kuti Vasiti asalowenso pamaso pa mfumu Ahasuwero; ndi mfumu aninkhe chifumu chake kwa mnzake womposa iye.


Kuthawira kwa Yehova nkokoma koposa kukhulupirira akulu.


Musamakhulupirira zinduna, kapena mwana wa munthu, amene mulibe chipulumutso mwa iye.


wakodwa ndi mau a m'kamwa mwako, wagwidwa ndi mau a m'kamwa mwako.


Siyani munthu, amene mpweya wake uli m'mphuno mwake; chifukwa m'mene awerengedwamo ndi muti?