Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Danieli 6:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Choncho mfumu Dariyo anasindikizapo dzina lake pa lamuloli.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

9 Momwemo mfumu Dariusi anatsimikiza cholembedwa ndi choletsacho.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Momwemo mfumu Dariusi anatsimikiza cholembedwa ndi choletsacho.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 6:9
6 Mawu Ofanana  

“Choncho, ngati chikukomerani mfumu, lamulirani kuti Vasiti asadzaonekerenso pamaso pa mfumu Ahasiwero. Lamuloli lilembedwe mʼmabuku a malamulo a Aperezi ndi Amedi kuti lisadzasinthike. Pamalo pa Vasiti ngati mfumukazi payikidwepo mkazi wina amene ali bwino kuposa iye.


Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova kusiyana ndi kudalira mafumu.


Musamadalire mafumu, anthu osakhalitsa, amene sangathe kupulumutsa.


ngati wagwidwa ndi zimene iwe unanena, wakodwa ndi mawu a mʼkamwa mwako.


Lekani kudalira munthu, amene moyo wake sukhalira kutha. Iye angathandize bwanji wina aliyense?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa