Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Afilipi 2:4 - Buku Lopatulika

munthu yense asapenyerere zake za iye yekha, koma yense apenyererenso za mnzake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

munthu yense asapenyerere zake za iye yekha, koma yense apenyererenso za mnzake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Musamangofuna zokomera inu nokha, koma zokomeranso anzanu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Musamangofuna zokomera inu nokha koma aliyense azifuna zokomeranso ena.

Onani mutuwo



Afilipi 2:4
15 Mawu Ofanana  

Koma chidadziwika ichi kwa Mordekai, ndiye anafotokozera Estere mkazi wamkulu; ndi Estere anamuuza mfumu, kumnenera Mordekai.


Ndipo Mose anati kwa ana a Gadi ndi ana a Rubeni, Kodi abale anu apite kunkhondo, ndi inu mukhale pansi kuno?


koma yense amene adzakhumudwitsa kamodzi ka tiana iti, takukhulupirira Ine, kumuyenera iye kuti mphero yaikulu ikolowekedwe m'khosi mwake, namizidwe poya pa nyanja.


Kondwani nao iwo akukondwera; lirani nao akulira.


Ndipo ife amene tili olimba tiyenera kunyamula zofooka za opanda mphamvu, ndi kusadzikondweretsa tokha.


Munthu asafune zake za iye yekha, koma za mnzake.


Afooka ndani wosafooka inenso? Akhumudwitsidwa ndani, wosatenthanso ine?


osapatsa chokhumudwitsa konse m'chinthu chilichonse, kuti utumikiwo usanenezedwe;


Pakuti onsewa atsata za iwo okha, si za Yesu Khristu.


Koma ngati muchita chikwanirire lamulolo lachifumu, monga mwa malembo, Uzikonda mnzako monga udzikonda wekha, muchita bwino: