Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Akorinto 10:24 - Buku Lopatulika

24 Munthu asafune zake za iye yekha, koma za mnzake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Munthu asafune zake za iye yekha, koma za mnzake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Munthu asamangodzifunira yekha zabwino, koma makamaka azifunira anzake zabwino.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Munthu aliyense asafunefune zokomera iye yekha, koma zokomeranso ena.

Onani mutuwo Koperani




1 Akorinto 10:24
7 Mawu Ofanana  

monga inenso ndikondweretsa onse m'zinthu zonse, wosafuna chipindulo changa, koma cha unyunjiwo, kuti apulumutsidwe.


sichichita zosayenera, sichitsata za mwini yekha, sichipsa mtima, sichilingirira zoipa;


Taonani, nthawi yachitatu iyi ndapukwa ine kudza kwa inu, ndipo sindidzakusaukitsani; pakuti sindifuna zanu, koma inu; pakuti ana sayenera kuunjikira atate ndi amai, koma atate ndi amai kuunjikira ana.


Pakuti onsewa atsata za iwo okha, si za Yesu Khristu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa