Afilipi 2:5 - Buku Lopatulika5 Mukhale nao mtima m'kati mwanu umene unalinso mwa Khristu Yesu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mukhale nao mtima m'kati mwanu umene unalinso mwa Khristu Yesu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Motero nonse mukhale ndi mtima womwe uja umene adaali nawonso Khristu Yesu: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pa ubale wanu wina ndi mnzake, mukhale ndi mtima wofanana ndi wa Khristu Yesu: Onani mutuwo |