Afilipi 2:6 - Buku Lopatulika6 ameneyo, pokhala nao maonekedwe a Mulungu, sanachiyese cholanda kukhala wofana ndi Mulungu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ameneyo, pokhala nao maonekedwe a Mulungu, sanachiyesa cholanda kukhala wofana ndi Mulungu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Iyeyu anali ndi umulungu chikhalire, komabe sadayese kuti kulingana ndi Mulungu ndi chinthu choti achigwiritsitse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iyeyu, pokhala Mulungu ndithu, sanatenge kufanana ndi Mulungu kukhala chinthu choyenera kuchigwiritsa. Onani mutuwo |