Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 22:15 - Buku Lopatulika

Ndipo Iye anatumiza mivi, nawawaza; mphezi, nawaopsa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Iye anatumiza mivi, nawawaza; mphezi, nawaopsa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaponya mivi yake, nabalalitsa adani ake. Adachititsa zing'aning'ani, naŵapirikitsa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anaponya mivi yake, nabalalitsa adani ake, ndi zingʼaningʼani zake anawagonjetsa.

Onani mutuwo



2 Samueli 22:15
8 Mawu Ofanana  

Ndipo anatuma mivi yake nawabalalitsa; inde mphezi zaunyinji, nawamwaza.


Mivi yanu njakuthwa; mitundu ya anthu igwa pansi pa inu; iwalasa mumtima adani a mfumu.


Dzuwa ndi mwezi zinaima njera mokhala mwao; pa kuunika kwa mivi yanu popita iyo. Pa kung'anipa kwa nthungo yanu yonyezimira.


Ndidzawaunjikira zoipa; ndidzawathera mivi yanga.


Ndipo Yehova anawamwaza pamaso pa Israele, ndipo anawakantha makanthidwe aakulu ku Gibiyoni, nawapirikitsa panjira yokwera pa Betehoroni, nawakantha mpaka Azeka, ndi mpaka Makeda.


Ndipo pamene Samuele analikupereka nsembe yopserezayo, Afilisti anayandikira kuti aponyane ndi Aisraele; koma tsiku lomwe lija Yehova anagunda ndi kugunda kwakukulu pa Afilistiwo, nawapolonganitsa. Ndipo anakanthidwa pamaso pa Aisraele.