Masalimo 45:5 - Buku Lopatulika5 Mivi yanu njakuthwa; mitundu ya anthu igwa pansi pa inu; iwalasa mumtima adani a mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mivi yanu njakuthwa; mitundu ya anthu igwa pansi pa inu; iwalasa mumtima adani a mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mivi yanu ndi yakuthwa, imalasa mitima ya adani. Mitundu ina ya anthu imagwa pansi pamaso panu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mivi yanu yakuthwa ilase mitima ya adani a mfumu, mitundu ya anthu igwe pansi pa mapazi anu. Onani mutuwo |