Masalimo 45:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo pindulani, mu ukulu wanu yendani, kaamba ka choonadi ndi chifatso ndi chilungamo; ndipo dzanja lanu lidzakuphunzitsani zoopsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo pindulani, m'ukulu wanu yendani, kaamba ka choonadi ndi chifatso ndi chilungamo; ndipo dzanja lanu lidzakuphunzitsani zoopsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pitani ndi ulemerero wanuwo, kuti mukagonjetse adani anu onse, mukateteze zimene zili zoona, zachifatso ndi zachilungamo. Dzanja lanu lamanja likaonetse ntchito zanu zoopsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mu ukulu wanu mupite mutakwera mwachigonjetso mʼmalo mwa choonadi, kudzichepetsa ndi chilungamo; dzanja lanu lamanja lionetsere ntchito zanu zoopsa. Onani mutuwo |