Masalimo 18:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo anatuma mivi yake nawabalalitsa; inde mphezi zaunyinji, nawamwaza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo anatuma mivi yake nawabalalitsa; inde mphezi zaunyinji, nawamwaza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Adaponya mivi yake nabalalitsa adani ake, adachititsa zing'aning'ani, naŵapirikitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Iye anaponya mivi yake nabalalitsa adani ake, ndi zingʼaningʼani zake anawagonjetsa. Onani mutuwo |