Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 22:12 - Buku Lopatulika

Ndipo anayesa mdimawo ngati mahema omzungulira Iye, kusonkhana kwa madzi ndi mitambo yochindikira ya mlengalenga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anayesa mdimawo ngati mahema omzungulira Iye, kusonkhana kwa madzi ndi mitambo yochindikira ya mlengalenga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mdima adausandutsa chofunda chake, mitambo yakuda yamvula adaisandutsa mwafuli wake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anapanga mdima kukhala chofunda chake, mitambo yakuda ya mlengalenga.

Onani mutuwo



2 Samueli 22:12
6 Mawu Ofanana  

Anaweramitsa miyambanso, natsika; ndipo mdima wandiweyani unali pansi pa mapazi ake.


Ndipo kunachitika, atamva Benihadadi mau awa, analikumwa nao mafumu m'misasa, ananena ndi anyamata ake, Nikani. Nandandalika pamzindapo.


Pali munthu kodi wodziwitsa mayalidwe a mitambo, ndi kugunda kwa msasa wake?


Chifukwa kuti pa tsiku la tsoka Iye adzandibisa mumsasa mwake, adzandibisa mkati mwa chihema chake; pathanthwe adzandikweza.


Pomzinga pali mitambo ndi mdima; chilungamo ndi chiweruzo ndizo zolimbitsa mpando wake wachifumu.