Masalimo 97:2 - Buku Lopatulika2 Pomzinga pali mitambo ndi mdima; chilungamo ndi chiweruzo ndizo zolimbitsa mpando wake wachifumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pomzinga pali mitambo ndi mdima; chilungamo ndi chiweruzo ndizo zolimbitsa mpando wachifumu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mitambo ndi mdima waukulu zamzinga Chauta. Amalamulira molungama, mu ufumu wake mulibe tsankho. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mitambo ndi mdima waukulu zamuzungulira; chilungamo ndi kuweruza molungama ndiwo maziko a mpando wake waufumu. Onani mutuwo |