Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 97:3 - Buku Lopatulika

3 Moto umtsogolera, nupsereza otsutsana naye pozungulirapo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Moto umtsogolera, nupsereza otsutsana naye pozungulirapo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Moto umapita patsogolo pake, umapsereza adani ake omzinga kulikonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Moto umapita patsogolo pake ndi kunyeketsa amaliwongo kumbali zonse.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 97:3
19 Mawu Ofanana  

Unakwera utsi wotuluka m'mphuno mwake, ndi moto wa m'kamwa mwake unanyeka nuyakitsa makala.


Ndipo Iye anaweramitsa thambo, natsika; ndipo pansi pa mapazi ake panali mdima bii.


Adzafika Mulungu wathu, ndipo sadzakhala chete. Moto udzanyeka pankhope pake, ndipo pozungulira pake padzasokosera kwakukulu.


Ndinapenya, ndipo taonani, mkuntho wa mphepo wochokera kumpoto, mtambo waukulu ndi moto wofukusika m'mwemo, ndi pozungulira pake padachita cheza, ndi m'kati mwake mudaoneka ngati chitsulo chakupsa m'kati mwa moto.


Mtsinje wamoto unayenda wotuluka pamaso pake, zikwizikwi anamtumikira, ndi unyinji wosawerengeka unaima pamaso pake, woweruza mlandu anakhalapo, ndi mabuku anatsegulidwa.


Patsogolo pake panapita mliri, ndi makala amoto anatuluka pa mapazi ake.


Pakuti taonani, likudza tsiku, lotentha ngati ng'anjo; ndipo onse akudzikuza ndi onse akuchita choipa. Adzakhala ngati chiputu; ndi tsiku lilinkudza lidzawayatsa, ati Yehova wa makamu, osawasiyira muzu kapena nthambi.


Pakuti wayaka moto mu mkwiyo wanga, utentha kumanda kunsi ukutha dziko lapansi ndi zipatso zake, nuyatsa maziko a mapiri.


Ndipo munayandikiza ndi kuima patsinde paphiri; ndi phirilo linayaka moto kufikira pakati pa thambo; kunali mdima, ndi mtambo, inde mdima bii.


Anakumvetsani mau ake kuchokera kumwamba, kuti akuphunzitseni; ndipo padziko lapansi anakuonetsani moto wake waukulu; nimunamva mau ake pakati pa moto.


Yehova ananena ndi inu popenyana maso m'phirimo, ali pakati pa moto,


m'lawi lamoto, ndi kubwezera chilango kwa iwo osamdziwa Mulungu, ndi iwo osamvera Uthenga Wabwino wa Ambuye wathu Yesu;


Pakuti Mulungu wathu ndiye moto wonyeketsa.


Ndipo wina akafuna kuipsa izo, moto utuluka m'kamwa mwao, nuononga adani ao; ndipo wina akafuna kuipsa izo, maphedwe ake ayenera kutero.


Ndipo ngati munthu sanapezedwe wolembedwa m'buku la moyo, anaponyedwa m'nyanja yamoto.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa