2 Samueli 22:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Iye anaberekeka pa kerubi nauluka; inde anaoneka pa mapiko a mphepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Iye anaberekeka pa kerubi nauluka; inde anaoneka pa mapiko a mphepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Adakwera pa mkerubi nauluka, adayenda mwaliŵiro ndi mphepo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iye anakwera pa Kerubi ndi kuwuluka; nawuluka ndi mphepo mwaliwiro. Onani mutuwo |