Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 22:13 - Buku Lopatulika

13 Cheza cha pamaso pake makala a moto anayaka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Cheza cha pamaso pake makala a moto anayaka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 M'kuŵala kumene kunali pamaso pake munkafumira makala amoto alaŵilaŵi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Mʼkuwala kumene kunali pamaso pake munkachokera makala amoto alawilawi.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 22:13
3 Mawu Ofanana  

Yehova anagunda kumwamba; ndipo Wam'mwambamwamba ananena mau ake.


M'mphuno mwake munatuluka utsi, ndi moto wotuluka m'kamwa mwake unaononga; makala anayaka nao.


Ndipo maonekedwe a ulemerero wa Yehova anali ngati moto wonyeketsa pamwamba paphiri, pamaso pa ana a Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa