Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yoweli 2:6 - Buku Lopatulika

Pamaso pao mitundu ya anthu ikumva zowawa, nkhope yonse zitumbuluka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamaso pao mitundu ya anthu ikumva zowawa, nkhope yonse zitumbuluka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu a mitundu ina amachita mantha akaŵaona, nkhope zonse zimatumbuluka.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Akangowaona, anthu a mitundu ina amazunzika mu mtima; nkhope iliyonse imagwa.

Onani mutuwo



Yoweli 2:6
7 Mawu Ofanana  

Popeza ndakhala ngati thumba lofukirira; koma sindiiwala malemba anu.


ndipo adzaopa; zowawa ndi masauko zidzawagwira; ndipo adzamva zowawa, ngati mkazi wakubala; adzazizwa wina ndi wina; nkhope zao zidzanga malawi a moto.


Funsani tsopano, ndi kuona ngati mwamuna aona mwana; chifukwa chanji ndiona mwamuna ndi manja ake pa chuuno chake, monga mkazi alinkubala, ndi nkhope zao zotumbuluka?


Bala la mwana wamkazi wa anthu anga ndaphwetekwa nalo; ndada mtima; kudabwa kwandigwira.


Maonekedwe ao ada koposa makala, sazindikirika m'makwalala; khungu lao limamatira pa mafupa ao, lakhwinyata, lasanduka ngati ndodo.


Ndiye mopanda kanthu mwakemo ndi mwachabe, ndi wopasuka; ndi mtima usungunuka, ndi maondo aombana, ndi m'zuuno zonse muwawa, ndi nkhope zao zatumbuluka.


Ili kuti ngaka ya mikango, ndi podyera misona ya mikango, kumene mkango, waumuna ndi waukazi, ukayenda ndi mwana wa mkango, kopanda wakuiposa?