Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:83 - Buku Lopatulika

83 Popeza ndakhala ngati thumba lofukirira; koma sindiiwala malemba anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

83 Popeza ndakhala ngati thumba lofukirira; koma sindiiwala malemba anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

83 Ndasanduka ngati thumba lachikopa lokhwinyata, komabe sindiiŵala malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

83 Ngakhale ndili ngati thumba lachikopa la vinyo pa utsi sindiyiwala zophunzitsa zanu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:83
6 Mawu Ofanana  

Khungu langa lada, nilindifundukira; ndi mafupa anga awawa ndi kutentha kwao.


Ndidzadzikondweretsa nao malemba anu; sindidzaiwala mau anu.


Ndinasochera ngati nkhosa yotayika; funani mtumiki wanu; pakuti sindiiwala malamulo anu.


Anandikulunga nazo zingwe za oipa; koma sindinaiwale chilamulo chanu.


Mphamvu yanga yauma ngati phale; ndi lilime langa likangamira kunsaya zanga; ndipo mwandifikitsa kufumbi la imfa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa