Yeremiya 8:21 - Buku Lopatulika21 Bala la mwana wamkazi wa anthu anga ndaphwetekwa nalo; ndada mtima; kudabwa kwandigwira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Bala la mwana wamkazi wa anthu anga ndaphwetekwa nalo; ndada mtima; kudabwa kwandigwira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Ndikumva kuŵaŵa chifukwa cha mavuto a anthu anga, ndikungolira, nkhaŵa yandigwira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Chifukwa cha mavuto a anthu anga, ine ndikumva kuwawa; ndikungolira ndipo mantha aakulu andigwira. Onani mutuwo |