Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Maliro 4:8 - Buku Lopatulika

8 Maonekedwe ao ada koposa makala, sazindikirika m'makwalala; khungu lao limamatira pa mafupa ao, lakhwinyata, lasanduka ngati ndodo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Maonekedwe ao ada koposa makala, sazindikirika m'makwalala; khungu lao limamatira pa mafupa ao, lakhwinyata, lasanduka ngati ndodo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Koma tsopano nkhope zao zasanduka zakuda ngati mwaye. Palibe amene akuŵazindikira m'miseu. Khungu lao lachita makwinyamakwinya, langoti gwa ngati mtengo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Koma tsopano maonekedwe awo ndi akuda kuposa mwaye; palibe angawazindikire mʼmisewu ya mu mzinda. Khungu lawo lachita makwinyamakwinya pa mafupa awo; lawuma gwaa ngati nkhuni.

Onani mutuwo Koperani




Maliro 4:8
17 Mawu Ofanana  

Fupa langa laumirira pa khungu langa ndi mnofu wanga, ndipo ndapulumuka ndili nazo nkhama za mano anga.


Ndipo pokweza maso ao ali kutali, sanamdziwe, nakweza mau ao, nalira; nang'amba yense malaya ake, nawaza fumbi kumwamba ligwe pamitu pao.


Khungu langa lada, nilindifundukira; ndi mafupa anga awawa ndi kutentha kwao.


Mnofu wake udatha, kuti sungapenyeke; ndi mafupa ake akusaoneka atuluka.


Masiku anga akunga mthunzi womka m'tali; ndipo ine ndauma ngati udzu.


Popeza ndakhala ngati thumba lofukirira; koma sindiiwala malemba anu.


Chifukwa usana ndi usiku dzanja lanu linandilemera ine; uwisi wanga unasandulika kuuma kwa malimwe.


Mumnofu mwanga mulibe chamoyo chifukwa cha ukali wanu; ndipo m'mafupa anga simuzizira, chifukwa cha cholakwa changa.


Monga ambiri anazizwa ndi iwe Israele, momwemo nkhope yake yaipitsidwa ndithu, kupambana munthu aliyense, ndi maonekedwe ake kupambana ana a anthu;


Khungu lathu lapserera ngati pamoto chifukwa cha kuwawa kwa njala.


Pamaso pao mitundu ya anthu ikumva zowawa, nkhope yonse zitumbuluka.


Ndiye mopanda kanthu mwakemo ndi mwachabe, ndi wopasuka; ndi mtima usungunuka, ndi maondo aombana, ndi m'zuuno zonse muwawa, ndi nkhope zao zatumbuluka.


Lingakhale fumbi lochokera kumudzi kwanu, lomamatika kumapazi athu, tilisansira pa inu; koma zindikirani ichi, kuti Ufumu wa Mulungu wayandikira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa