Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 7:53 - Buku Lopatulika

Ndipo anamuka munthu yense kunyumba yake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anamuka munthu yense kunyumba yake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo anthu onse adabwerera kwao.]

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka onse anachoka, napita kwawo.

Onani mutuwo



Yohane 7:53
7 Mawu Ofanana  

Yehova aphwanya upo wa amitundu, asandutsa chabe zolingirira za mitundu ya anthu.


Indedi, kuzaza kwake kwa munthu kudzakulemekezani; chotsalira cha kuzazaku mudzachiletsa.


Olimba mtima chifunkhidwa chuma chao, agona tulo tao; amuna onse amphamvu asowa manja ao.


Anayankha nati kwa iye, Kodi iwenso uli wotuluka mu Galileya? Santhula, nuone kuti mu Galileya sanauke mneneri.


Koma Yesu anamuka kuphiri la Azitona.


ndi kulawirana; ndipo tinalowa m'ngalawa, koma iwo anabwera kwao.