Masalimo 33:10 - Buku Lopatulika10 Yehova aphwanya upo wa amitundu, asandutsa chabe zolingirira za mitundu ya anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Yehova aphwanya upo wa amitundu, asandutsa chabe zolingirira za mitundu ya anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Zolinga za anthu akunja Chauta amazisandutsa zopandapake. Maganizo ao onse amaŵasandutsa achabechabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Yehova amalepheretsa chikonzero cha anthu a mitundu ina; Iye amaphwanya zolinga za anthu ambiri. Onani mutuwo |