Machitidwe a Atumwi 21:6 - Buku Lopatulika6 ndi kulawirana; ndipo tinalowa m'ngalawa, koma iwo anabwera kwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndi kulawirana; ndipo tinalowa m'ngalawa, koma iwo anabwera kwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndipo titatsazikana, ife tidakaloŵa m'chombo, iwowo nkumabwerera kwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Titatsanzikana, tinalowa mʼsitima ija, iwowo anabwerera ku nyumba zawo. Onani mutuwo |