Yohane 7:52 - Buku Lopatulika52 Anayankha nati kwa iye, Kodi iwenso uli wotuluka mu Galileya? Santhula, nuone kuti mu Galileya sanauke mneneri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201452 Anayankha nati kwa iye, Kodi iwenso uli wotuluka m'Galileya? Santhula, nuone kuti m'Galileya sanauke mneneri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa52 Iwo adati, “Kani iwenso ndiwe wa ku Galileya? Kafunefune m'Malembo ndipo udzaona kuti palibe mneneri wochokera ku Galileya.” [ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero52 Iwo anayankha kuti, “Kodi ndiwenso wochokera ku Galileya? Tayangʼananso, ndipo udzapeza kuti mneneri sachokera ku Galileya.” Onani mutuwo |