Yohane 7:51 - Buku Lopatulika51 Kodi chilamulo chathu chiweruza munthu, osayamba kumva iye, ndi kuzindikira chimene achita? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Kodi chilamulo chathu chiweruza munthu, osayamba kumva iye, ndi kuzindikira chimene achita? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 “Kodi Malamulo athu amatilola kuweruza munthu tisanamve mau ake kuti tidziŵe zimene wachita?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 “Kodi lamulo lathu limatsutsa munthu popanda kumva mbali yake kuti tipeze chimene wachita?” Onani mutuwo |