Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 7:50 - Buku Lopatulika

50 Nikodemo ananena kwa iwo, amene uja adadza kwa Iye kale, ali mmodzi wa iwo,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

50 Nikodemo ananena kwa iwo, amene uja adadza kwa Iye kale, ali mmodzi wa iwo,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

50 Tsono Nikodemo, mmodzi mwa Afarisi, yemwe uja amene kale adaapita kwa Yesu, adafunsa anzakewo kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

50 Nekodimo, amene anapita kwa Yesu poyamba paja ndipo anali mmodzi wa iwo, anafunsa kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yohane 7:50
4 Mawu Ofanana  

Adzandiukira ndani kutsutsana nao ochita zoipa? Adzandilimbikira ndani kutsutsana nao ochita zopanda pake?


Koma anadzanso Nikodemo, amene anadza kwa Iye usiku poyamba paja, alikutenga chisakanizo cha mure ndi aloe, monga miyeso zana.


Koma khamu ili losadziwa chilamulo, likhala lotembereredwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa