Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 7:53 - Buku Lopatulika

53 Ndipo anamuka munthu yense kunyumba yake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

53 Ndipo anamuka munthu yense kunyumba yake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

53 Pamenepo anthu onse adabwerera kwao.]

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

53 Kenaka onse anachoka, napita kwawo.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 7:53
7 Mawu Ofanana  

Yehova aphwanya upo wa amitundu, asandutsa chabe zolingirira za mitundu ya anthu.


Indedi, kuzaza kwake kwa munthu kudzakulemekezani; chotsalira cha kuzazaku mudzachiletsa.


Olimba mtima chifunkhidwa chuma chao, agona tulo tao; amuna onse amphamvu asowa manja ao.


Anayankha nati kwa iye, Kodi iwenso uli wotuluka mu Galileya? Santhula, nuone kuti mu Galileya sanauke mneneri.


Koma Yesu anamuka kuphiri la Azitona.


ndi kulawirana; ndipo tinalowa m'ngalawa, koma iwo anabwera kwao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa