Masalimo 76:10 - Buku Lopatulika10 Indedi, kuzaza kwake kwa munthu kudzakulemekezani; chotsalira cha kuzazaku mudzachiletsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Indedi, kuzaza kwake kwa munthu kudzakulemekezani; chotsalira cha kuzazaku mudzachiletsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Zoonadi, mkwiyo wa anthu umabweretsa ulemu kwa Inu, opulumuka ku mkwiyowo mumaŵasunga pafupi ndi Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Zoonadi, ukali wanu pa anthu umakubweretserani matamando ndipo opulumuka ku ukali wanu mumawasunga pafupi nanu. Onani mutuwo |