Masalimo 76:9 - Buku Lopatulika9 pakuuka Mulungu kuti aweruze, kuti apulumutse ofatsa onse a padziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 pakuuka Mulungu kuti aweruze, kuti apulumutse ofatsa onse a pa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 pamene Inu Mulungu mudaimirira kuti muweruze anthu, ndi kupulumutsa opsinjidwa onse a pa dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 pamene Inu Mulungu munadzuka kuti muweruze, kupulumutsa onse osautsidwa mʼdziko. Sela Onani mutuwo |