Masalimo 76:8 - Buku Lopatulika8 Mudamveketsa chiweruzo chochokera Kumwamba; dziko lapansi linachita mantha, nilinakhala chete, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Mudamveketsa chiweruzo chochokera Kumwamba; dziko lapansi linachita mantha, nilinakhala chete, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chiweruzo chanu mudachilengeza kumwamba, anthu a pa dziko lapansi adaopa nakhala chete, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Kuchokera kumwamba Inu munalengeza chiweruzo, ndipo dziko linaopa ndi kukhala chete, Onani mutuwo |